Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb19 May tsamba 4
  • Paulo Anali ndi “Munga M’thupi”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Paulo Anali ndi “Munga M’thupi”
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
  • Nkhani Yofanana
  • Anthu Okhulupirika Analimbana ndi Minga M’matupi Awo
    Nsanja ya Olonda—2002
  • Kulimbana ndi “Munga M’thupi”
    Nsanja ya Olonda—2002
  • Kufooka kwa Anthu Kusonyeza Mphamvu ya Yehova
    Nsanja ya Olonda—1997
  • Kodi Muli ndi “Munga m’Thupi”?
    Utumiki Wathu wa Ufumu—1998
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
mwb19 May tsamba 4

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | 2 AKORINTO 11-13

Paulo Anali ndi “Munga M’thupi”

12:7-10

Nthawi zambiri Baibulo likamanena za munga kapena kuti minga, limanena za anthu kapena zinthu zosowetsa mtendere komanso zomwe zingavulaze munthu wina. (Num. 33:55; Miy. 22:5; Ezek. 28:24) Pamene Paulo ankalemba kuti anali ndi “munga m’thupi,” ayenera kuti ankanena za atumwi achinyengo komanso anthu ena omwe ankamusokoneza pa ntchito yake monga mtumwi. Kodi malemba otsatirawa akusonyeza zinthu zina ziti zomwe zinali ngati “munga m’thupi” kwa Paulo?

  • Mtumwi Paulo wagwira mutu

    Mac. 23:1-5

  • Agal. 4:14, 15

  • Agal. 6:11

Kodi inuyo mukulimbana ndi vuto lotani?

Mungasonyeze bwanji kuti mumadalira Yehova kuti akuthandizeni kupilira?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena