Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 120
  • Khalani Omvera Kuti Mulandire Madalitso

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Khalani Omvera Kuti Mulandire Madalitso
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Mvera Kuti Udalitsidwe
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Kodi Ndinu ‘Okonzeka Kumvera’?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2023
  • Akamvera Adzapeza Moyo
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Akamvera Adzapeza Moyo
    Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 120

Nyimbo 120

Khalani Omvera Kuti Mulandire Madalitso

Losindikizidwa

(Luka 11:28)

1. Kodi ndife anthu omvera Khristu

Pa zonse zimene ananena?

Kuzidziwa n’kosangalatsa ndithu.

Tidalitsidwa tikazimvera.

(KOLASI)

Mvera udalitsidwe

Kuti usangalale.

Zomwe Mulungu angakuuze

Mvera udalitsidwe.

2. Monga nyumba yomangidwa pathanthwe

Osati yomangidwa pamchenga,

Zochita zathu zingatiteteze

Kokha ngati Yesu timumvera.

(KOLASI)

Mvera udalitsidwe

Kuti usangalale.

Zomwe Mulungu angakuuze

Mvera udalitsidwe.

3. Monga mtengo wamumbali mwa madzi

Umabereka nthawi ’kafika,

Tikamvera tidzadalitsidwadi

Moyo wosatha tidzalandira.

(KOLASI)

Mvera udalitsidwe

Kuti usangalale.

Zomwe Mulungu angakuuze

Mvera udalitsidwe.

(Onaninso Deut. 28:2; Sal. 1:3; Miy. 10:22; Mat. 7:24-27.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena