Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 122
  • Khamu la Abale

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Khamu la Abale
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Abale Ambirimbiri
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Unyinji wa Abale
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Tsoka Lachiwiri Linali Makamu a Asilikali Okwera Pamahatchi
    Mapeto Osangalatsa a Masomphenya a M’buku la Chivumbulutso
  • Zimene Muyenera Kudziwa Zokhudza Angelo
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawira)—2017
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 122

Nyimbo 122

Khamu la Abale

Losindikizidwa

(Chivumbulutso 7:9, 10)

1. Abale ambirimbiri,

Inde ochuluka,

Aliyense ndi mboni

Yokhulupirika.

Tilipodi ambiri,

Tikuchulukabe.

Tachokeratu ku mafuko

Ndi mitundu yonse.

2. Abale ambirimbiri,

Timalalikira

Uthenga wabwinodi

Kwa ofuna kumva.

Ngakhale tingatope,

Yesu atipatsa

Mpumulo ndi mphamvu zambiri.

Tidzasangalala.

3. Abale ambirimbiri,

Otetezedwadi,

Otumikira M’lungu

Padziko lapansi.

Tilipodi ambiri,

Timalalikira,

Timagwira ntchito ndi

M’lungu Pomutumikira.

(Onaninso Yes. 52:7; Mat. 11:29; Chiv. 7:15.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena