Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 112
  • Yehova, Mulungu Wamkulu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yehova, Mulungu Wamkulu
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Yehova Mulungu Wamkulu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • ‘Atate Wanu Ndi Wachifundo’
    Nsanja ya Olonda—2007
  • Kodi Mudzatsanzira Chifundo cha Mulungu?
    Nsanja ya Olonda—1991
  • “Njira Zake Zonse Ndi Zolungama”
    Yandikirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 112

Nyimbo 112

Yehova, Mulungu Wamkulu

Losindikizidwa

(Ekisodo 34:6, 7)

1. Inu Yehova M’lungu wamkulu

Ndinu woyeneradi

Kutamandidwa zedi.

Ndinu wabwino ndi wolungama.

Ndinu M’lungu kosatha.

2. Mumakhululukiradi anthu

Amene monga inu

Ndi achifundo ndithu.

Mumasonyeza kukoma mtima

Pa zonse mumachita.

3. Mutamandidwe ndi anthu onse

Dzina lanu liyere

Wina asalikane.

Dziko lapansi likhale mmene

Inu mumafunira.

(Onaninso Deut. 32:4; Miy. 16:12; Mat. 6:10; Chiv. 4:11.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena