Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 60
  • Mulungu Adzakupatsani Mphamvu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mulungu Adzakupatsani Mphamvu
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Adzakulimbitsa
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Tikhale Ndi Chikhulupiriro Cholimba
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Kukonzekera Kupita Kokalalikira
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Kukonzekera Kupita Kolalikira
    Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 60

Nyimbo 60

Mulungu Adzakupatsani Mphamvu

Losindikizidwa

(1 Petulo 5:10)

1. Panali chifukwa chimene Mulungu

Anakupatsira choonadi

Anaona mtima wofuna kuchita

Zabwino zomukondweretsadi.

Unalonjeza kum’tumikira

Ndipo Iye anakuthandiza

(KOLASI)

Ndi magazi a Yesu Anakuwombola

Adzakulimbitsa adzakuteteza.

Adzakutsogolera ndi mzimu woyera

Adzakulimbitsa adzakuteteza.

2. Mulungu anapereka mwana wake

Amafunadi zikuyendere.

Ngati mwana wakeyo sanatimane

Kukulimbitsa sangalephere.

Chikondi chako sangaiwale

Sangasiye konse anthu ake.

(KOLASI)

Ndi magazi a Yesu Anakuwombola

Adzakulimbitsa adzakuteteza.

Adzakutsogolera ndi mzimu woyera

Adzakulimbitsa adzakuteteza.

(Onaninso Aroma 8:32; 14:8, 9; Aheb. 6:10; 1 Pet. 2:9.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena