Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 82
  • “Muzionetsa Kuwala Kwanu”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Muzionetsa Kuwala Kwanu”
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • “Onetsani Kuwala Kwanu”
    Imbirani Yehova
  • ‘Muwalitse Kuunika Kwanu’
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2001
  • “Onetsani Kuwala Kwanu”
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
  • “Onetsani Kuwala Kwanu” Kuti Yehova Alemekezeke
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2018
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 82

NYIMBO 82

“Muzionetsa Kuwala Kwanu”

Losindikizidwa

(Mateyu 5:​16)

  1. 1. Yesu walamula

    Kuti tiwale.

    Monga dzuwa

    limawalira onse,

    Nafe tifikire

    Anthu onsewo.

    Choncho tizisonyeza

    Kuwala kwake.

  2. 2. Uthenga wa M’lungu

    ufalikire.

    Uzitiwalira

    Polalikira.

    Tiphunzitse anthu

    Choonadichi.

    Anthu asankhe okha

    Kumva uthenga.

  3. 3. Tikamasonyeza

    Kukoma mtima

    Timawalitsadi

    Dziko la mdima.

    Choncho tisonyeze

    Kuwala kwathu.

    Tikatero Mulungu

    Asangalala.

(Onaninso Sal. 119:130; Mat. 5:​14, 15, 45; Akol. 4:6.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena