Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 121
  • Chowonadi Chimene Chimamasula Anthu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Chowonadi Chimene Chimamasula Anthu
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • “Choonadi Chidzakumasulani”
    Nsanja ya Olonda—1998
  • Akristu Amalambira Mumzimu ndi M’choonadi
    Nsanja ya Olonda—2002
  • Kutsanzira Mulungu wa Choonadi
    Nsanja ya Olonda—2003
  • Kodi Nkufuniranji Choonadi?
    Nsanja ya Olonda—1995
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 121

Nyimbo 121

Chowonadi Chimene Chimamasula Anthu

(Yohane 8:32)

1. Chilamulo cha Mose ndi ulosi wakale

Zinasonya ku cho’nadi chimene tidziŵa.

Ndicho cho’nadi chomasula, cha Mbewu ya Ya

—Mmene anthu angapezere moyo mwa Yesu.

2. ‘Ndine njira, chowonadi,’ Yesu ananena.

Anadza m’dziko kufera machimo a anthu,

Kuzadziŵitsa dzina la Atate wowona

‘Nthaŵi ya mapeto’ kugonjetsa adaniwo.

3. Kupyolera mwa Mwana wa Ya cho’nadi chadza.

Chimatitsimikiza za kutha kwa uchimo.

Ndiye Mbewu, Wolonjezedwa kutama M’lungu.

Monga Mfumu ndi Wansembe alamula tsono.

4. Ndi chikhulupiliro tilalika za Mwana.

Takonzekera kulengeza mbiri yabwino.

Ufumu Waumesiyawo tichirikize.

Tiusonyeze kwa onse agwirire ntchito.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena