Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 112
  • Ndipo Adzadziŵa

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndipo Adzadziŵa
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Yehova, Nyonga Yathu ndi Mphamvu Yathu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Yehova Ndi Mphamvu Yathu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Yehova Ndiye Mphamvu Yathu
    Imbirani Yehova
  • Iri Nditsiku la Yehova
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 112

Nyimbo 112

Ndipo Adzadziŵa

(Ezekieli 35:15)

1. Adaniwo anyoza dzinalo,

Mwachinyengo adetsa malowo.

Msanga Mfumu imveketsa zanu;

Ufumu wa Satana udzatha.

(Korasi)

2. Satanayo, apeputsa mphamvu,

Idzatuluka osakanidwa.

Khamu lake, pa Armagedoyo,

Lidzafika pakuwonongedwa.

(Korasi)

3. Odzikweza nkhaza kwa ofatsa

Afuna kuma lamulirabe.

Dzanja lanu lidzathyola goli.

Oputa mkwiyo wanu adzatha.

(KORASi)

Adzadziŵa inu nokha Yehova;

Kuti njira zanu nzolungama.

Adzadziŵa muchilengedwe chonse,

Chifuno chanu mudzachichita.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena