Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 76
  • Yehova, Bwenzi Lathu Labwino Kopambana

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yehova, Bwenzi Lathu Labwino Kopambana
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Yehova Akhoza Kukhala Mnzanu
    Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale—Kuphunzira Baibulo Mokambirana
  • Mulungu Akukuitanani Kuti Mukhale Bwenzi Lake
    Mungathe Kukhala Bwenzi la Mulungu!
  • Kodi Baibulo Limanena Zotani pa Nkhani Yokhala Ndi Anzathu?
    Kuyankha Mafunso a M’Baibulo
  • Anzanu Azikhala Anthu Amene Amakonda Yehova
    Kodi Mungatani Kuti Mulungu Azikukondani?
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 76

Nyimbo 76

Yehova, Bwenzi Lathu Labwino Kopambana

(Yesaya 41:8)

1. Yehova Wodalirika,

Ndibwenzi lathudi.

Anapanga dziko lathu,

Napereka moyo.

Makolowo anakana

Njira ya Yehova,

Ali bwenzi la omvera

Ofuna tsikulo.

2. Munthu wokhulupirika

Ndiye Abrahamu.

Yehova atamuyesa,

Iye sanasinthe.

Anadziŵa kuti mwana

Wake adzauka.

Ya anakonda Abra’mu,

Wosunga umphumphu.

3. Yesu anadza kudziko

Chifukwa cha anthu.

Anatitayira moyo

Kutiyanjanitsa.

Satana anayesadi

Kupatutsa Yesu,

Monga wokhulupirika,

Anali wowona.

4. Palibe bwenzi loposa

Yehova ndi Kristu.

Anasonyeza chikondi

Chopezetsa moyo.

Ubwenzi ndi dziko ndiwo

Udani ndi M’lungu.

Tisonyezedi kukhala

Mabwenzi owona.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena