Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 36
  • “Achimwemwe Ali Ofatsa”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Achimwemwe Ali Ofatsa”
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Ngachimwemwe Chotani Nanga Ofatsa!
    Nsanja ya Olonda—1991
  • Tsanzirani Khristu Pokhala Anthu Ofatsa
    Imbirani Yehova
  • Yesetsani Kukhala Ofatsa Kuti Muzisangalatsa Yehova
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2019
  • ‘Kondwerani mwa Yehova’
    Nsanja ya Olonda—2003
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 36

Nyimbo 36

“Achimwemwe Ali Ofatsa”

(Mateyu 5:5, NW)

1. M’lungu adalitsa ofatsa;

Chimwemwe nchachikuludi.

Ngakhale amasautsidwa;

Modekha alinda M’lungu.

Sada nkhawa ndi oipa,

Odzitukumula onse.

Amadziŵa kuti iwowa,

Adzafa ngati maudzu.

2. “Kuyambira ubwana wanga,

Tsopano ine ndakula.

Sindinawone wolungama

Akumapempha chakudya.”

Yendani mowongokabe

Khulupilirani M’lungu.

Mukakondwera mwa Yehova,

Ntchito yanu idzadala.

3. Oipa adzatha padziko;

Sadzawonanso pokhala,

Ofatsa adzasangalala

Ndi mtendere wochuluka.

Kufikira kunthaŵiyo

Tisunge Mawu a M’lungu,

Tikumasonyeza chifatso

Muzochita zathu zonse.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena