Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 52
  • Dzina la Atate Wathu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Dzina la Atate Wathu
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Dalitsani Ubale Wathu Wachikristu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Chikondi cha Mulungu Chokhulupirika
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Chifukwa cha Kukondwera cha Ziyoni
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Moyo Wosatha Ulonjezedwa
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 52

Nyimbo 52

Dzina la Atate Wathu

(Mateyu 6:9)

1. Yehova inu Wamkulu,

Yeretsani dzina lo.

Muchite chifuno chanu,

Lileke kudetsedwa.

Lidzayeretsedwa msanga,

Mwa chilakiko chanu.

Kulitsani mbiri yanu;

Onse alabadire.

(Korasi)

2. Tifunanso kuyeretsa

Dzina lanu loyera;

Tilankhula molimbika

Za zifuno zanuzo.

Mwa kukhulupiriraku,

Tikulemekezani.

Tikhulupiriketu kwa

Atate Woyeranu.

(Korasi)

3. O Ambuye Yehovanu,

Ndinu Wammwambamwamba.

Palibe china choposa

Kukulemekezani.

M’dzina lanu timaguba;

Tifuna kusonyeza

Kuti ndinu wa chifuno

Mudzadalitsidwadi.

(KORASI)

Mfumu ndinu Mpangi wathu;

Chilengedwechi nchanu,

Poti ndinu Mulungudi

Wokwanitsa zifuno.

Yehova munapereka

Mwana wanu wayekha,

M’chite chifuniro chanu,

Padziko lapansili.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena