Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 58
  • Yehova, “Mulungu wa Chitonthozo Chonse”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yehova, “Mulungu wa Chitonthozo Chonse”
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Chitonthozo Chochokera kwa “Mulungu wa Chitonthozo Chonse”
    Nsanja ya Olonda—1995
  • Tonthozani Amene ali ndi Chisoni
    Nsanja ya Olonda—2003
  • ‘Tonthozani Anthu Onse Olira’
    Nsanja ya Olonda—2011
  • Kodi Mulungu Amatilimbikitsa Bwanji?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawira)—2016
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 58

Nyimbo 58

Yehova, “Mulungu wa Chitonthozo Chonse”

(2 Akorinto 1:3-7)

1. Mulungu amatonthozadi;

Amatikonda zedi.

Titonthoze ena ndi Mawu,

Pansi pa Yesu Kristu.

2. Lero mavuto ngochuluka;

Tonse timawapeza.

Koma Yehova atonthoza,

Pokhala mboni zake.

3. Adalitsike Yehovayo;

Timalimbikitsidwa.

Adzatitsitsimula ndithu

Ngati tipilirabe.

4. Tonse tingapezedi mphamvu,

Poloŵa mumavuto.

Yesu anaphunzitsa kuti:

M’lungu amatikonda.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena