Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 68
  • Chifundo Chaumulungu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Chifundo Chaumulungu
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Tizitsanzira Yehova pa Nkhani ya Chifundo
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2017
  • “Chifundo Chachikulu cha Mulungu Wathu”
    Yandikirani Yehova
  • Khalani ndi Mtima Wachifundo
    Nsanja ya Olonda—1994
  • Sonyezani ‘Chifundo Chachikulu’
    Nsanja ya Olonda—2007
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 68

Nyimbo 68

Chifundo Chaumulungu

(Akolose 3:12)

1. Tikakhaladi Akristu,

Tisonyeze chifundo

Kwa mabwenzi ndi alendo,

Ndi kwa osawadziŵa.

Yesu Mphunzitsiyo

Anamveketsa izi

Mwafanizo lake.

Odala akumvawo.

2. ‘Msamariya winawake

Anamka ku Yeriko.

M’njira anapeza Myuda;

Wofwambidwa panjira.’

Kuti amthandize,

Anachotsa kunyada.

Mwachikondi chake.

Anachita lamulo.

3. Izi zisonyeza mnansi.

Wofuna chithandizo.

Ya ndi wabwino kwa onse,

Apatsa mvula dzuŵa.

Chikondi chakecho!

Ndithudi bwenzi lathu.

Kukoma mtimako.

Pa izi tidalira.

4. Nthaŵi zina tipereka

Chakudya kwa mnansidi.

Kulidi kofulumira,

Kuti apeze moyo.

Kudziŵa Ufumu,

Cho’nadi cha Mulungu

Tipatsa anansi

Kuti atamande Ya.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena