Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 147
  • Chuma Chosalephera

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Chuma Chosalephera
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Tizichita Zinthu Zogwirizana Ndi Dzina Lathu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Zochita Zathu Zizigwirizana ndi Dzina Lathu
    Imbirani Yehova
  • Ntchito Yomwe Tagwira Chifukwa cha Chikondi
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Ntchito Imene Tagwira Chifukwa cha Chikondi
    Imbirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 147

Nyimbo 147

Chuma Chosalephera

(Mateyu 6:20)

1. Tate wakumwamba, tikuthokoza

Kuti tadziŵa cho’nadi!

Ndimwaŵi kulengeza za

Ufumu Ndi kuti uli pafupi!

2. Nzeru, chilungamo, mphamvu, chikondi

Zimasonkhezera mtima.

Kukhala ndi Yesu Mpulumutsiyo,

Kumatipatsa chimwemwe.

3. Ubwenzi wathu nanu ndidalitso.

Tingakhumbenso chiyani?

Chifundo chanu chipatsa mtendere

Umenedi timafuna.

4. Tiri ndi chifukwa choyamikira;

Mawuwo adzapambana.

Mupatsa chiyanjo kwa okondedwa.

Ndi chuma chosalephera.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena