Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 184
  • Abusa Achikondi Ayang’anira “Nkhosa”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Abusa Achikondi Ayang’anira “Nkhosa”
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Abusa Omwe Ndi ‘Zitsanzo kwa Gulu’ la Nkhosa
    Nsanja ya Olonda—2006
  • Kuŵeta Nkhosa Zamtengo Wake za Yehova Mokoma Mtima
    Nsanja ya Olonda—1993
  • “Abusa Amene Mtima Wanga Wakonda”
    Zimene Mulungu Akutiuza Kudzera mwa Yeremiya
  • Amaŵeta Nkhosa Mwachifundo
    Nsanja ya Olonda—1993
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 184

Nyimbo 184

Abusa Achikondi Ayang’anira “Nkhosa”

(1 Petro 5:2)

1. Ambuye tikuthokoza,

Muli Mbusa wamkulu.

Mutisunga mwachikondi.

Mutetezera “nkhosa.”

2. Yesu anapatsa ’busa

Amatidera nkhaŵa.

Adzipereka muntchito,

Kuphunzitsa cho’nadi.

3. Abusa a gulu la Ya,

Mufunire ubwino.

Mulithandize kukula,

Kuti liwonjezeke.

4. Polalikira pamodzi,

Timalimbikitsidwa!

Tidzatumikira M’lungu,

Ndi kusonyeza changu.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena