Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 134
  • ‘Chitani Monga Amuna’

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • ‘Chitani Monga Amuna’
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Kugonjetsa Dziko
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Nyimbo Yachilakiko
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Gwirizanani Nawo m’Nyimbo Yaufumu!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Tiimbile Limodzi Nyimbo ya Ufumu
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 134

Nyimbo 134

‘Chitani Monga Amuna’

(1 Akorinto 16:13)

1. ‘Ona mwamuna!’ ati Pilato.

Ndithu Yesu ndi chitsanzo chabwino!

Ndi kulimba mtima analaka

Dziko la Satana la udanili.

2. Yesu anakhazika chitsanzo.

Tikhale monga mmene analiri.

Poyang’anana ndi Armagedo,

Tilimbe mtimatu; monga amuna.

3. Kulimba kuli kofunikadi

Kwa okhulupirika onse a Ya.

Pomwe mapeto ayandikira,

Tilimbebe mu ntchito ya Ufumu.

4. Atumiki onse a Yehova,

Amayang’ana kwa Yesu Mfumuyo.

Mosawopa khalani amphamvu.

Nyimbo yolakika adzaiimba.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena