Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 187
  • Zinthu Zonse Zipangidwa Kukhala Zatsopano

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zinthu Zonse Zipangidwa Kukhala Zatsopano
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Zinthu Zonse Zidzakhala Zatsopano
    Imbirani Yehova
  • “Zinthu Zonse Zimene Ndikupanga Ndi Zatsopano”
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Moyo Wosatha Ulonjezedwa
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 187

Nyimbo 187

Zinthu Zonse Zipangidwa Kukhala Zatsopano

(Chivumbulutso 21:4)

1. Zinthu zisonya M’lungu alamula.

Pa mpando wakhala Mwana wake.

Munkhondo yam’mwamba walakika,

Ndipo kwatsala dziko lapansi.

(Korasi)

2. Anthu awone Yerusalemuyo,

Mkwatibwi wa Mwanawankhosayo.

Wovekedwa tsono mokongola,

Yehova ndiye kuŵala kwake.

(Korasi)

3. Mzindawu udzasangalatsa anthu.

Ndi zipata zake zosatseka.

Anthu adzayenda mu ku’nika.

Gaŵirani kunyezimirako.

(KORASi)

Kondwa. Chifukwa Mulungu

Alitu ndi anthu ake.

Sikudzakhalanso kulira,

Pena zopweteka ndi imfa;

Zidzakhala zatsopano zonse.

Odalirika mawu.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena