Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 168
  • Kuzindikira Mfumu Yatsopano ya Dziko Lapansi

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kuzindikira Mfumu Yatsopano ya Dziko Lapansi
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Moyo Wosatha Ulonjezedwa
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Lonjezo la Mulungu la Paradaiso
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Kuyenda Muumphumphu
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 168

Nyimbo 168

Kuzindikira Mfumu Yatsopano ya Dziko Lapansi

(Salmo 2:12)

1. Tawonani padzikoli

Chondikondweretsadi—

Gulu lake la Yehova

Muumodzi liyenda.

Zisoti zawo ziŵala,

Ndi kuchotsatu zolakwa.

Afuula molimbika:

“Kristu alamulira.”

(Korasi)

2. Mfumu Kristu, atsogoza;

Ndipo amamtsatira.

Ponena iye amvera

Kulibenso chisoni.

Lupanga lakuthwa Mawu.

Avala iwo mbiriyo.

Amlondola Mbuye wawo;

Kufikira kuimfa.

(Korasi)

3. Tsono nthaŵi yafikatu

Yakulamula Yesu.

Adani onse adzagwa;

Nadzagwidwa ndi mantha.

Yehova achita mphamvu.

Ndi kulizanso lipenga.

Chenjerani mafumunu;

Etu muvomereze.

(KORASi)

Mpsopsonenitu Mwanayo

Kuti mungatayike.

Achimwemwetu

okhulupilira iye!

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena