Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 162
  • “Lalika Mawu”!

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Lalika Mawu”!
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • “Lalikira Mawu”
    Imbirani Yehova
  • “Lalikira Mawu”
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Tilalikire Mbiri Yabwino Imeneyi Yaufumu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Ndi Ndani Amene Amalalikira Uthenga Wabwino?
    Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale—Kuphunzira Baibulo Mokambirana
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 162

Nyimbo 162

“Lalika Mawu”!

(2 Timoteo 4:2)

1. ‘Lalikirani Mawuwo,’

Walamula leroli.

Ife tapatsidwa nthaŵi

Kumvera lamulolo.

“Lalika” ndi kuphunzitsa;

Thandizani ofo’ka.

Lalikabe, osawopa

Pamakwalala ponse.

2. “Lalika” munyengo yonse,

Wokonzeka kuyankha

Aliyense wakufunsa

Chiyembekezo chathu.

“Lalika” mopanda nyengo

Otsutsa alekeni.

Khala wokhulupirika;

Kwa M’lungu wamkuluyo.

3. “Lalika” mosalekeza.

Onse chonde amvetu!

Kuipa kuli kukula

Mapeto akufika.

“Lalika” mupulumuke

Inu ndi anthu ena.

“Lalika,” nthaŵi yafika

Kutamanda Yehova.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena