Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 131
  • Kumamatira kwa Yehova Mulungu Wathu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kumamatira kwa Yehova Mulungu Wathu
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Timamatire Yehova
    Imbirani Yehova
  • Chipatso cha Kudziletsa
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Mulungu Wamkulu, Yehova!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • “Yehova Mulungu Wathu Ndi Yehova Mmodzi”
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2016
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 131

Nyimbo 131

Kumamatira kwa Yehova Mulungu Wathu

(Yoswa 23:8)

1. Ife a “nyumba” ya M’lungu timtumikira;

Timasunga kudzipereka kwapadera.

Tatopa ndi milungu ya mitunduyi.

Timamatira Ya; timutumikire.

Asonkhezere cho’nadi mumtimamo.

2. Zinthu za lonjezo, zimene ananena,

Zikhala zowona—chitsenderezo chitha!

Ufumu womadza udzathetsa nkhondo.

Timamatirabe; tiwonjeze mbiri.

Ndi Mulungu wathu; adzetsa mtendere.

3. Bukhu la chowonadi tiliŵerengedi.

Timamamatira Ya ndi kumvera Mawu.

Tifuna kumkonda ndi kumtumikira.

Chifuno chake tichikhulupilire

Kulambira kwake kuli kofunika.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena