Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 143
  • Imani ndi Yehova!

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Imani ndi Yehova!
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Khalani ku Mbali ya Yehova
    Imbirani Yehova
  • Khalani Kumbali ya Yehova
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Yehova, Nyonga Yathu ndi Mphamvu Yathu
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 143

Nyimbo 143

Imani ndi Yehova!

(Eksodo 32:26)

1. Kale tinalitu achisoni,

Kumwa za chipembedzo chonyenga;

Koma mwachimwemwe tadzutsidwa

Pakumva za Ufumu (Ufumu).

(Korasi)

2. Ndi mtima wonse timtumikire

Kugaŵana cho’nadi ponsepo,

Kuthandizira abale onse,

Kutama dzina lake (lakelo).

(Korasi)

3. Sitidzamuwopa Satanayo,

Yehova adzatipulumutsa.

Tingachepe iwo nachuluka,

M’lungu ndi mphamvu yathu (yathudi).

(KORASi)

Ima kwa Yehova; Musekerere.

Sadzakusiyani; Yenda mwa iye.

Nenani mbiriyo Ya ufuluwo.

Kulamula kwake Sikudzathadi.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena