Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 77
  • “Yehova ndi Mbusa Wanga”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Yehova ndi Mbusa Wanga”
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • “Yehova Ndi M’busa Wanga”
    Imbirani Yehova
  • “Yehova Ndi M’busa Wanga”
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Yehova Ndi Mbusa Wathu
    Nsanja ya Olonda—2005
  • “Ndine Pano! Munditumize Ine”
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 77

Nyimbo 77

“Yehova ndi Mbusa Wanga”

(Salmo 23)

1. Yehova ndi Mbusa wanga;

Kodi ndingawopenji?

Pakuti wosamala nkhosa

Sadzaiŵala zake.

Anditengera kumadzi,

Moyo wanga upuma.

Atsogoza mapazi anga

M’njira za chilungamo.

Atsogoza mapazi anga

M’njira za chilungamo.

2. Nkana munthunzi wa imfa

Ndiyenda wosawopa,

Mbusa wanga ali pafupi;

Kumanditonthozabe.

Amandidzoza mafuta;

Wadzaza chikho changa.

Ukoma wake unditsate,

Ndikhale m’nyumba yake.

Ukoma wake unditsate,

Ndikhale m’nyumba yake.

3. Wachikonditu mbusayo!

Ndimtamanda moimba.

Mbiri yake yosangalatsa

Kwa nkhosa ndidzanena.

Mawu ake ndidzatsata,

Poyenda m’njira yake.

Chuma changa chomtumikira

Ndigwiritsira ntchito.

Chuma changa chomtumikira

Ndigwiritsira ntchito.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena