Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 53
  • Kuwonjezeka kwa Teokrase

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kuwonjezeka kwa Teokrase
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Khalanibe m’Teokrase
    Nsanja ya Olonda—1998
  • Yehova Alamulira—Kupyolera mwa Teokrase
    Nsanja ya Olonda—1994
  • Kuyamikira Kudekha kwa Mulungu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Ufumu wa Yehova Wayamba Kulamulira
    Imbirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 53

Nyimbo 53

Kuwonjezeka kwa Teokrase

(Yesaya 9:6, 7)

1. Tama Teokrase wowonjezeka!

Kukula kwake kukuchitika.

Chitamando cha Yehova nchosatha

Kwa oyenda m’kuunika kwake.

Panali chiyambi chochepa pomwe

Mombolo anayenda padziko.

Tsopano “Otsalira” ndi khamulo

Atamanda Mfumu ya Mulungu.

2. Kristu pachimpando alamulira;

Anthu aima pamaso pake.

Adzakweza Ufumu wa Mulungu,

Powonongatu adani ake.

Phungu Wodabwitsa ndi Wautate,

Wamphamvu, Kalonga waMtendere.

Yehova adzabweretsa mtendere

Ufumu wake nuwonjezeka.

3. Amwaŵi ife pokhala ndi moyo!

Mukondwe nacho chiwonjezeko.

Khalanibe ndi chimwemwe m’kupatsa,

Khalani ndi phande muumboni.

Chenjezani onyoza dzina la Ya;

Kuti Armagedo yayandika.

Mwachangu ubukitseni Ufumu

Kwa ofatsa ndi ousa moyo.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena