Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 14
  • ‘Kondwerani, Anthu Inu’!

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • ‘Kondwerani, Anthu Inu’!
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Tizisangalatsa Mtima wa Yehova
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Tikondweretse Mtima wa Yehova
    Imbirani Yehova
  • Kukondweretsa Mtima wa Yehova
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Ana Amene Amakondwereta Mtima wa Yehova
    Nsanja ya Olonda—1987
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 14

Nyimbo 14

‘Kondwerani, Anthu Inu’!

(Aroma 15:10)

1. Kondwerani, ndi anthu ake!

Ufumu wayamba.

Kristu wakhala mu Ziyoni;

Kondwerani konse!

Nthaŵi za akunjazo zatha;

Tsiku lawo latha.

Kondwerani, ndi anthu ake!

Mfumu ilamula.

2. Kondwerani, ndi anthu ake!

Dongosolo litha

Nkhondo ya’magedo iridi

Pafupi kwambiri.

Anthu potamanda chonyansa

Pokana Kalonga,

Ife titama Kalongayo;

Adzawonjezeka.

3. Kondwerani, ndi anthu ake!

Nenani pakhomo

Mbiri yabwino ya Ufumu;

Lengezani ponse

Kristu alamula mwanzeru,

Ndiponso m’chikondi.

Kondwerani, ndi anthu ake!

Mtumikirenitu.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena