Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 72
  • Zisangalalo ndi Zipatso za Utumiki Waufumu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zisangalalo ndi Zipatso za Utumiki Waufumu
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Kukwaniritsa Zofunika za Mulungu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Pezani Chimwemwe mwa Kukhala Wopatsa!
    Nsanja ya Olonda—2001
  • Tilalikire Mbiri Yabwino Imeneyi Yaufumu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Kondwerani m’Chiyembekezo cha Ufumu!
    Nsanja ya Olonda—1991
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 72

Nyimbo 72

Zisangalalo ndi Zipatso za Utumiki Waufumu

(Mateyu 5:12)

1. Muutumiki wa M’lungu wathu,

Mulidi chimwemwe choposa,

Pakuti tilalikira mbiri

Kuti ena atonthozedwe.

Yesu anatitsimikizira:

Kupatsa kudzetsa chimwemwe.

Ndipo kodi tingaperekenji

Koposa chowonadi cha kumoyo.

2. Ngakhale pomka khomo ndi khomo

Tipeza onyoza ndi mphwayi,

Tisunga chitsimikizo chathu

Ndi kugwiritsa umphumphuwo.

Ngati tikumana ndi chizunzo

Pochiriki za dzina la Ya,

Yesu anatitu tikondwere,

Aneneriwo anavutikanso.

3. Utumikiwo ngwosangalatsa

Potsatira njira ya Mbuye;

Lalika za tsiku la Yehova

Ndi kulemekeza Yehova!

Tiwadzetsera chiyembekezo

Cha dziko lopanda uchimo.

Izi zitipatsa chikhutiro,

Chiyembekezo cha moyo wosatha.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena