Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 6
  • Lengezani Mbiri Yabwino Yosatha

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Lengezani Mbiri Yabwino Yosatha
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Angelo Angakuthandizeni Bwanji?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawira)—2017
  • Mbiri Yabwino Kaamba ka Mtundu Wonse wa Anthu!
    Nsanja ya Olonda​—1990
  • Tilalikire Mbiri Yabwino Imeneyi Yaufumu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Nchifukwa Ninji Tiyenera Kuwopa Mulungu?
    Nsanja ya Olonda—1989
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 6

Nyimbo 6

Lengezani Mbiri Yabwino Yosatha

(Chivumbulutso 14:6-8)

1. Kuzungulira dziko mngelo wa M’lungu,

Auluka mmwamba ndi mbiri yabwino.

Ati: ‘Opani Mfumu iri pampando.

Inde, lambirani Yehova yekhayo.

Tsono ora lachiweruzo lafika,

Posachedwa oipa adzachotsedwa.’

Alaliki a Ufumu asawope

Alankhule mwamphamvu mbiri ponsepo.

2. Mngelo wachiŵiri akulengezanji

Kuti, ife Mboni za Ya tigaŵane?

Anena za kugwa kwa Babulo mkulu,

Kuti posachedwa adzawonongedwa.

Potero Ya alamula tibukitse

Kulipsira ndi kukwezedwa kwa dzina.

Munda tilalikira ngwaukuludi;

Koma mngelo wa Mulungu atsogoza.

3. “Mwana wa munthu” pamodzi ndi angelo

Wayambatu kuweruza amitundu.

Dana nacho choipa. Konda chabwino.

Opa M’lungu ndi kusunga malamulo.

Thayo loikidwa kwa ife ndi ’mbuye

Ndiro kulalikira mbiri yabwino.

Chotero ife tilangiza molimba,

“Idzani kudzalambira Ya mokondwa.”

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena