Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 130
  • Utumiki Wosangalatsa

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Utumiki Wosangalatsa
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Muzigwira Nawo Mokwanira Ntchito Yokolola Mwauzimu
    Nsanja ya Olonda—2010
  • Mfumu Yosatha, Yeretsani Dzina Lanu!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Achimwemwe, Ngachifundo!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Akristu Amapeza Chimwemwe Potumikira
    Nsanja ya Olonda—2000
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 130

Nyimbo 130

Utumiki Wosangalatsa

(Salmo 32:11)

1. Mokondwa titumikire Mfumuyo,

Podza nazo mphatso kuntchito yake.

Nkana utumikiwo ukachepa

Chikondi chathu chikuwonekera.

2. Ntchito ya Yehova iri kwa onse,

Antchito alikuitanidwabe.

Talandira ntchito yopatulika;

Madalitso adza mwa ntchito yathu.

3. Nkana anthu akane chowonadi,

Tidziŵa kuti “M’lungu sanganame.”

Motero tilalikire Mawuwo,

Chifukwa mwa iwo timadalira.

4. Pogaŵana mokondwa muntchitoyo

Timachitira umboni kwa onse,

Chifukwa M’lungu wathu atiyanja,

Watipanga kukhala atumiki.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena