Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 64
  • Chikhulupiliro Chonga Chija cha Abrahamu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Chikhulupiliro Chonga Chija cha Abrahamu
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Abulahamu Anasonyeza Kuti Anali Wokhulupirika
    Zimene Tingaphunzire Munkhani za M’Baibulo
  • Abulahamu Anali “Bwenzi” la Yehova
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2016
  • Mulungu Ayesa Abrahamu
    Bukhu Langa la Nkhani za Baibulo
  • Kodi Abulahamu Anali Ndani?
    Nsanja ya Olonda—2012
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 64

Nyimbo 64

Chikhulupiliro Chonga Chija cha Abrahamu

(Genesis 22:1-18)

1. Ngwodala wozindikira

Mawu a Mulungu;

Poti Mulungu adziŵa

Poyamba mapeto.

Kutitonthoza ifeyo,

Mwa anthu akale

Anachita maulosi,

Omveka tsopano.

2. Tawonani Abrahamu,

Ndi Isake naye,

Ali m’Phiri la Moriya;

Ali kuyesedwa.

Yehova anamupempha

Kupatsa mwana’ke

Kuti chifuno cha M’lungu

Chikwaniritsidwe.

3. Abrahamu anatero,

Nakhala chitsanzo

Kuti M’lungu adzatuma

Dipo Mwana wake.

Kodi mukufuna moyo?

Khalani womvera,

Khalani wokhulupira

Monga Abrahamu.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena