Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 128
  • Chitani Zochuluka—Monga Anaziri

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Chitani Zochuluka—Monga Anaziri
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Mungatsanzire Bwanji Anaziri?
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • Zimene Tingaphunzire kwa Anaziri
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2024
  • Mfundo Zazikulu za M’buku la Numeri
    Nsanja ya Olonda—2004
  • Mafunso Ochokera kwa Owerenga
    Nsanja ya Olonda—2005
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 128

Nyimbo 128

Chitani Zochuluka—Monga Anaziri

(Numeri 6:8)

1. Anaziri—Tiwatsanzire?

Kodi tingateronso?

Opatulidwira Yehova

Munjira yapadera.

Pendani! Tikusamalire.

Nthaŵi ikutha mwamsanga.

Kodi tingawonjezere

Utumiki wathu?

2. Anaziri—Moyo wawotu

Unali wodzikana.

Unawadzetsa kwa Mulungu.

Kodi tingateronso?

Analola ziletso zina;

Za kulumbira kwawoko.

Abale athu ambiri

Achita motero.

3. Anaziri—Anasiyana

Anali apadera.

Anachitadi mogonjera;

Anamvera Mulungu.

Monga antchito a Mulungu

Tiri ndi chikhulupiro.

Mulungu atidalitse,

Tichitetu changu.

4. Anaziri—Ngachitsanzodi.

Anali osamala.

Tikhaletu osadetsedwa;

Ya anawadalitsa.

Daliranitu Yehovayo.

Asamala anthu ake.

Tichite zambiri ndithu

Tipeze chimwemwe.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena