Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 40
  • Kupanga Njira Yathu Kukhala Yachipambano

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kupanga Njira Yathu Kukhala Yachipambano
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Khalani ndi Moyo Wopambana
    Imbirani Yehova
  • Kukonzekera Kupita Kokalalikira
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Kukonzekera Kupita Kolalikira
    Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Titeteze Mtima Wathu
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 40

Nyimbo 40

Kupanga Njira Yathu Kukhala Yachipambano

(Yoswa 1:8)

1. M’lungu anauza Yoswa:

‘Khalabe m’Lamulo.

Uŵerenge nthaŵi zonse,

Ulisamalire.

Likutsogozetu m’zonse,

Likhalebe mkamwa (ndithudi).

Udzapambana, cho’nadi

Chidzakutsogoza (zo’nadi).’

Udzapambana, cho’nadi

Chidzakutsogoza.

2. Mafumu mu Israyeli

Analamulidwa:

‘Adzilembere Lamulo

La Mulungu mwini,

Naŵerenge nthaŵi zonse

Nadzichepetsetu (indedi).’

Ya akamuwonjezera;

Masiku ambiri (ambiri).

Ya akamuwonjezera;

Masiku ambiri.

3. M’Baibulo timapeza

Zofuna za M’lungu.

Poti sitingadzipende,

Atithandizetu.

Tikamvera mawu ake

Tidzamdziŵa ndithu (o inde).

M’lungu akatiphunzitsa,

Tidzasunga mawu (akewo).

M’lungu akatiphunzitsa,

Tidzasunga mawu.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena