Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 93
  • Malo Abwino a Yehova Olambiliramo

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Malo Abwino a Yehova Olambiliramo
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Loŵani m’Mabwalo a Kachisi wa Yehova!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Gwirizanani Nawo m’Nyimbo Yaufumu!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Tiimbile Limodzi Nyimbo ya Ufumu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Tiyeni Tiimbe Nyimbo ya Ufumu!
    Imbirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 93

Nyimbo 93

Malo Abwino a Yehova Olambiliramo

(Salmo 84:1)

1. Kachisi wanu ngwabwino,

Atumiki aimamo!

Moyo wanga ufunatu,

Kuti ndi kaimbiremo,

Kuti ndikaimbiremo.

2. Yehova podza kwa inu

Kukonzanso mphamvu zathu,

Mutidyetsa ndi cho’nadi,

Titumikire mwamphamvu,

Titumikire mwamphamvu.

3. Tsiku m’mabwalo anutu

Liposa zikwi kwinanso.

Tikhaletu m’nyumba yanu

Koposa ndi oipawo,

Koposa ndi oipawo.

4. Yehova nditchinjirizo

Kwa onse olungamawo.

Samawamana zabwino

Osalakwa m’nkhola lake,

Osalakwa m’khola lake.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena