Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 100
  • Tamani Yehova Mulungu Wathu!

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tamani Yehova Mulungu Wathu!
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • “Chimwemwe Chimene Yehova Amapereka”
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Tamandani Yehova, Mulungu Wathu!
    Imbirani Yehova
  • Chimwemwe Chimene Yehova Amapereka
    Imbirani Yehova
  • Tamandani Yehova Mulungu Wathu
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 100

Nyimbo 100

Tamani Yehova Mulungu Wathu!

(Yeremiya 33:11)

1. Tamani! Yehova M’lungu!

Dziŵitsanitu! Ukulu!

Fu’lani! Nyimbo yokondwa!

Dziko ndi kumwamba ndizake.

Zinthu zonse anazipanga.

Zisonyeza mphamvu yake.

Nzeru chilungamo nzambiri;

Ziri zogwirizanadi!

Tamani! Yehova M’lungu!

Dziŵitsanitu! Ukulu!

2. Tamani! Yehova M’lungu!

Dziŵitsanitu! Ubwino!

Fu’lani! Ngwokoma mtima!

Wona ni kukoma mtimako.

Wochititsa mantha munkhondo,

Kwa ofatsa ngwabwinodi.

Ateteza omufunawo.

Apeza kukoma mtima.

Tamani! Yehova M’lungu!

Dziŵitsanitu! Ubwino!

3. Tamani! Yehova M’lungu!

Dziŵitsanitu! Ufumu!

Mveketsa! Ukulu wa Ya

Kungodya zonse zadzikoli!

Nthaŵi yadza! Kristu ndi Mfumu.

Tiyamiketu Yehova.

Tiimbe nyimbo yolakika,

Tisonyeze chidaliro.

Tamani! Yehova M’lungu!

Dziŵitsanitu! Ufumu!

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena