Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 209
  • Tsatirani Mfumu Yankhondo!

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tsatirani Mfumu Yankhondo!
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Nyimbo kwa Wammwambamwambayo
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Tiimbile Limodzi Nyimbo ya Ufumu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Tiyeni Tiimbe Nyimbo ya Ufumu!
    Imbirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 209

Nyimbo 209

Tsatirani Mfumu Yankhondo!

(Aefeso 6:16, 17)

1. Tiri nayo nyimbo ya kwa Yehova;

Yaulemelero ndi ufumu.

Tiri ndi uthenga wa anthu amve

Ndi ulamuliro wa kunena.

(Korasi)

2. Ankhondo a Mulungu, dzukanitu

Pansi pa Ngwazi ya a ufulu;

Tengani chikopa cha ku uzimu,

Ndi chisoti cha chipulumutso.

(Korasi)

3. Sitingapambane mumphamvu yathu;

Mwa tokha sitingathe nkhondoyo.

Koma mwa Mulungu tinga pambane,

Kudziŵitsa dzina la Yehova.

(KORASI)

Pitani! (Inde!)

Musawope! (Musawope!)

Monga gulu lankhondo

Lomenyana ndi mdani;

Tsatira ni Kristu Mfumu yankhondo.

Mtsatireni, tidzalaka!

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena