Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 48
  • Tamani Yehova

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tamani Yehova
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Tiyenera Kukhala Mtundu Wanji wa Anthu?
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Tizichita Zinthu Zogwirizana Ndi Dzina Lathu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Zochita Zathu Zizigwirizana ndi Dzina Lathu
    Imbirani Yehova
  • Ntchito Yomwe Tagwira Chifukwa cha Chikondi
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 48

Nyimbo 48

Tamani Yehova

(1 Akorinto 3:7)

1. Tamani Yehova.

M’chikondi chake

Mwapatsidwa ntchito

Younikira.

Palibenso chomwe

Simulandira

Kwa M’lungu wanuyo;

Mumlemekeze.

2. M’kwezeni iyeyo;

Dzichepetseni.

Tero mudzaŵala

Ndi za kumwamba.

Yenda mwa Iyeyo,

Mumfunefune,

Mukumatsogoza

Ntchito yakeyo.

3. Mukatu mokondwa

Kumtumikira;

Thokozadi zonse

Aperekazi.

Tamatu Yehova,

Lalikiratu,

Kufikira onse

Amlemekeze.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena