Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 34
  • Kukhala ndi Moyo Mogwirizana ndi Dzina Lathu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kukhala ndi Moyo Mogwirizana ndi Dzina Lathu
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Zochita Zathu Zizigwirizana ndi Dzina Lathu
    Imbirani Yehova
  • Tizichita Zinthu Zogwirizana Ndi Dzina Lathu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Ntchito Yomwe Tagwira Chifukwa cha Chikondi
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Ntchito Imene Tagwira Chifukwa cha Chikondi
    Imbirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 34

Nyimbo 34

Kukhala ndi Moyo Mogwirizana ndi Dzina Lathu

(Yesaya 43:10-12)

1. Yehova, wamphamvuyonse, wamyaya,

Wosayerekezeka m’chikondi,

Magwero a chowonadi ndi nzeru,

Inu mulamula monga Mfumu.

Angelo akondwera m’ntchito yanu;

Chilengedwe chinena za inu.

Mwatcha ife kukhala Mboni zanu;

Tigwirizane ndi dzina lathu!

2. Mutithandize, M’lungu nthaŵi zonse

Kulilemekeza dzina lanu,

Kuziwongolera mphatso za ntchito

Posamala malangizo anu.

Tikasamale mayendedwe athu,

Kuti chitonzo china chisadze.

Amwaŵidi pokhala Mboni zanu;

Tigwirizane ndi dzina lathu!

3. Pokhalabe muutumiki wanu,

Limodzi mtendere ndi chikondi,

Chikhutiro chikhala gawo lathu;

Potamandanu tisangalala.

Tigwirizane ndi dzina lathulo;

Kuuza cho’nadi kwa’nthu onse;

Ndipo koposa zonse chikondwero,

Kumtima wanu, Yehova Mfumu!

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena