Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 43
  • Patsogolo, Inu Aminisitala Aufumu!

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Patsogolo, Inu Aminisitala Aufumu!
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Pitani Patsogolo, Inu Atumiki a Ufumu!
    Imbirani Yehova
  • Pitirizani Kulalikira za Ufumu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Pitani Patsogolo Mboninu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Pitani Patsogolo Mboninu!
    Imbirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 43

Nyimbo 43

Patsogolo, Inu Aminisitala Aufumu!

(2 Timoteo 4:5)

1. Lalikiranibe Ufumu

Kwa anthu onse m’dziko.

Mwachikondi cha paanansi,

Thandizani ofatsa.

M’kulemekeza utumiki

Tisamale mavalidwe.

Uministala ngwapamwamba;

Tifuna kudalitsa Ya.

(Korasi)

2. Aministala atsopano

Pitani patsogolo.

Muiŵale zomwe mwasiya,

Pezani nyonga mwa Ya.

Monga zotengera za M’lungu

Musiyane ndi dzikoli.

Anthu a M’lungu ayenera

Kusiya njira zadziko.

(Korasi)

3. Tonse tipite patsogolo,

Otsalira ndi “nkhosa.”

Amuna, akazi, ndi ana,

Tiyende m’chowonadi.

Ntchito yathu njopatulika

Tifuna kuiyeretsa.

Imatonthoza olungama

Nalemekeza Yehova.

(KORASI)

Pitanibe,

Falitsani Ufumu kulikonse.

Khalanibe

Okhulupirika kwa Yehovayo.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena