Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 67
  • Kundikani Chuma Mmwamba

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kundikani Chuma Mmwamba
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Tili ndi Chuma Chamtengo Wapatali Chofunika Kugawira Ena
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2008
  • Fufuzani Chuma Chimene ‘Chinabisidwa Mosamala mwa Iye’
    Nsanja ya Olonda—2009
  • Pezani Chimwemwe mwa Kukhala Wopatsa!
    Nsanja ya Olonda—2001
  • Pulogalamu Yatsopano ya Msonkhano Wadera
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2007
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 67

Nyimbo 67

Kundikani Chuma Mmwamba

(Mateyu 6:20)

1. Timukondetu Yehova,

Tate wa mauniko!

Mphatso zonse zabwinozi,

Zichokera kwa iye.

Zovala, chakudya, mbewu,

Nthaka, dzuŵa ndi mvula.

Tiyamikire Mgaŵiri;

Asunga moyo wathu.

2. Ndikupusa kumataya

Nthaŵi yathu mudyera,

Kuunjika chuma chino,

Chosatipatsa moyo!

Tikhale okhutira ndi

Zinthu zofunikadi,

Mwantchito zathu zabwino

Tigwirire moyodi.

3. Tigwiritse nthaŵi yathu

Kuwadyetsa “amphaŵi,”

Kupatsa “anjala” mbiri

Yabwino ya Ufumu.

Mwautumiki tikhala

Abwenzi a Mulungu;

Kusonkhanitsira m’mwamba

Chuma cha umuyaya.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena