Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 71
  • Gwiritsitsani Mbiri Yabwino!

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Gwiritsitsani Mbiri Yabwino!
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Khalani Olimba, Osasunthika
    Imbirani Yehova
  • Khalani Okhazikika, Osasunthika!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Khalani Okhazikika Kuti Mudzapambane pa Mpikisano wa Moyo
    Nsanja ya Olonda—2003
  • Yehova Ndi Mphamvu Yathu
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 71

Nyimbo 71

Gwiritsitsani Mbiri Yabwino!

(1 Akorinto 15:2)

1. Tikhazikike muntchito,

Pofika mapeto.

Monga abale tichite,

Modalira M’lungu.

Kuŵala kwa chowonadi,

Tichita zambiri.

Ntchito yathu siri chabe

—Ikondweretsadi.

2. Chiukiriro cha anthu

Chidzutsa mitima,

Chiwathandiza kulimba.

Chiwakondweretsa.

Tifuna kukhulupira

Malonjezo a Ya.

Tiimetu molimbika;

Kuti tipambane.

3. Pogwira ntchito mwamphamvu

Kufika mapeto,

Tifunetu atsamwali

Otilimbikitsa.

“Mbiri” ya chiyembekezo

Cha Paradaiso.

Tiyamikira Mulungu

Mwa Mwana’ke Kristu.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena