Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 113
  • Ndife Mboni za Yehova!

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndife Mboni za Yehova!
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Ndife Mboni za Yehova!
    Imbirani Yehova
  • Ndife Mboni za Yehova
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Moyo Wosatha Ulonjezedwa
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 113

Nyimbo 113

Ndife Mboni za Yehova!

(Yesaya 43:10-12)

1. Anthu amapangadi

Milungu ya mitengo.

Iye ndi Mulungu

Wamphamvuyonse.

Milungu sikhozatu

Kuwona zamtsogolo.

Afunatu mboni mwachabe,

Milunguyo sithandiza.

(Korasi)

2. ‘Ndinu mboni Zangadi,

Musawope milungu.

Ndinetu Yehova,

Mfumu ndi Mbuye.

Ine ndipulumutsa.

Palibe M’lungu wina.

Lengezanibe dzina langa;

Muli inu mboni zanga.’

(Korasi)

3. Kulengeza dzinalo,

Lichotsedwe chitonzo.

Chenjeza onyoza

Dzina la M’lungu.

Kuti a khulukira,

Anthu onse olapa.

Kulalikira kubweretsa

Chiyembekezo chamoyo.

(KORASI)

Mbonife za Yehova;

Tilankhula molimba.

Wathu ndi M’lungu waulosi;

Amanena zowona.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena