Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 37
  • Kupanga Dzina Labwino ndi Mulungu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kupanga Dzina Labwino ndi Mulungu
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Kukonzekera Kupita Kokalalikira
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Kukonzekera Kupita Kolalikira
    Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Tipange Mbiri Yabwino kwa Mulungu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Phunziro 3
    Zimene Ndikuphunzira M’Baibulo
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 37

Nyimbo 37

Kupanga Dzina Labwino ndi Mulungu

(Mlaliki 7:1)

1. Tifunitsitsa

Chiyanjo cha M’lungu.

Timafunadi

Kumkondweretsabe.

Dzina labwinodi,

Monga tadziŵira,

Tingalipange,

Tiyenera.

2. Mwamawu athu

Tingapeze dzina.

Tikulipanga,

Poti tilifuna.

Tikamka kwa M’lungu,

Tidzapeza dzina

Labwinodi ndi

Madalitso.

3. Tipanga dzina

Momvera Mulungu.

Pokhala moyo,

Izi nzofunika.

Tikatetezera

Mawu Ake ndithu

Adzakhaladi

Bwenzi lathu.

4. Nthaŵi nzoipa,

Tichitepo kanthu,

Kupanga dzina

Ndi Ya, M’lungu wathu.

Tichite zabwino,

Tiyende m’kuŵala

Tifalitse

za Ufumuwo.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena