Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 189
  • Kulengeza Tsiku Lakubwezera la Yehova

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kulengeza Tsiku Lakubwezera la Yehova
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Tsiku Lakubwezera la mulungu
    Nsanja ya Olonda—1991
  • “Ine Ndakuika Kuti Ukhale Mlonda”
    Yehova Wabwezeretsa Kulambira Koyera
  • Tsanzirani Yesu mwa Kulalikira Molimba Mtima
    Nsanja ya Olonda—2009
  • Kodi Mumalalikira Molimba Mtima?
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2000
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 189

Nyimbo 189

Kulengeza Tsiku Lakubwezera la Yehova

(Yesaya 61:2)

1. Malipenga amveka;

Chi’tano chamveka.

Tsiku lobwezeralo

La Ya layandika.

Tilengeza molimba,

Nkana anyozera.

Tipereke chenjezo;

Ufumu wabadwa.

2. Nkhondoyo nja Yehova.

Yesu atsogoza.

Mapeto olakika,

Kukweza cho’nadi.

Maluso a Satana

Adzathetsedwadi.

Taphunzitsidwa ndi

Ya Kumenya nkhondoyo.

3. Alonda achenjeza.

Afu’la pamodzi.

Yenseyo m’malo ake

Mwa kufuna kwa Ya.

Yehova ali n’nthaŵi;

Nthaŵiyo ikutha

Kuti tilalikire

Za Ufumu wake.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena