Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 81
  • Kuyamikira Kudekha kwa Mulungu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kuyamikira Kudekha kwa Mulungu
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Bwerani kwa Mulungu Kuti Mupulumuke
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Bwerani kwa Mulungu Kuti Mupulumuke
    Imbirani Yehova
  • Yehova Ndi Mphamvu Yathu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Yehova Ndiye Mphamvu Yathu
    Imbirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 81

Nyimbo 81

Kuyamikira Kudekha kwa Mulungu

(2 Petro 3:15)

1. Yehova mphamvu yanuyo

Inapanga zokongola.

Ponseponse chilengedwe

Chimalengeza za ichi.

Ngakhale kukongolako

Kusangalatsa abwino,

Adzawona kukongola

M’chilakiko cha ufumu.

2. Chilungamo chanu M’lungu

Chingathe kuipa konse;

Kutitu tipulumuke,

Simunawonongeretu.

Otchedwa ndi dzina lanu,

Aimba moyamikira

Nafunitsitsa kuwona

Chilakiko cha ufumu.

3. M’chipiliro chanu M’lungu

Tilalikira mbiriyo,

Kusonyeza ’nthu ubwino,

Wopezeka m’Mawu anu.

Mutithandize kunena

Kutinso apulumuke

Pamodzi nafe awone

Ufumu wolakikawo.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena