Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 1
  • ‘Lemekeza Yehova, O Moyo Wanga’

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • ‘Lemekeza Yehova, O Moyo Wanga’
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • “Lemekeza Yehova, Moyo Wanga”
    Nsanja ya Olonda—1999
  • Yehova Amafunikira Chitamando Chosatha
    Nsanja ya Olonda​—1990
  • Okhulupirika Anu Adzakulemekezani
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Mudalitse Msonkhano Wathu
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 1

Nyimbo 1

‘Lemekeza Yehova, O Moyo Wanga’

(Salmo 103)

1. N’dzalemekeza Yehova—

Milomo yanga imyimbire—

Iye amakhululuka,

Nachotsadi chisoni chonse.

Sakwiya msanga, ngwachifundo,

Zonse zimtsimikizira.

Onse owopa Yehova,

Adzaŵakomera mtima.

2. Yehova ngwachifundodi,

Adziŵa kuti ndife fumbi

Monga duŵa la kuthengo,

Ndimo mmene timafotera.

Iye ndimfumu pazonse;

Ntchito zake ziri zamphamvu.

Tika sunga malangizo,

Adzatichirimikitsa.

3. Yehova anakhazika

Mpando wachifumu kumwamba.

Koma ukoma wa Yehova

Ngwa onse omamumvera.

Mdalitse Yehova angelo;

Mkwezeni ndi mtima wonse.

M’dalitse Yehova nonse.

Dalitsa M’lungu mtimanga.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena