Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 208
  • Nyimbo ya Chikondwelero

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Nyimbo ya Chikondwelero
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Nyimbo kwa Wammwambamwambayo
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Lonjezo la Mulungu la Paradaiso
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Tiimbile Limodzi Nyimbo ya Ufumu
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 208

Nyimbo 208

Nyimbo ya Chikondwelero

(Chivumbulutso 11:15)

1. Timva mphalasa.

Chisangalalo.

Mwana wa M’lungu alamula.

Nsanje zilira.

Nsalu ziŵala.

Mfu’yo imveka dziko lonse:

(Korasi)

2. Mwa kulalika

ndi kuphunzitsa,

Ambiri adza kwa Yehova.

Amaimbanso

Mosangalala,

Zikumamveka konsekonse!

(Korasi)

3. Tichitirane

Mwachikondidi

Anthu a Mulungu abale.

Kuimba kwathu

Kuwonje zebe

Chitamandocho kwa Yehova.

(KORASi)

Tsikuli ndi la Ya. (Idzani.)

Ufumu sudzatha. (Kondwa.)

Chinthu chiri chonse (Kondwani.)

Tamani M’lungu muimbe:

‘Kwa Ya tipeza chipulumutso

Ndi Kristu yemwe ali Mfumu.’

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena