Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 122
  • Kudzisungira Ife Eni Monga “Wamng’ono”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kudzisungira Ife Eni Monga “Wamng’ono”
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Yesetsani Kukhala Ngati Wamng’ono
    Nsanja ya Olonda—2012
  • Dalitsani Kusonkhana Kwathu Pamodzi
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Ubwino Wogonjera Anthu Amene Akutitsogolera M’gulu la Mulungu
    Gulu Lochita Chifuniro cha Mulungu
  • Paradaiso Wathu: Tsopano ndi Mtsogolo
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 122

Nyimbo 122

Kudzisungira Ife Eni Monga “Wamng’ono”

(Luka 9:48)

1. Oyanjidwadi ndi awo

Omvera malangizo.

Ntchito ya odalira Ya

Imadalitsidwadi.

Popeza tivutika ndi

Kusalungama kwathu,

Tifune kudzichepetsa

Tigonjere Mulungu.

2. ‘Dzichepetsenitu nokha,’

Kristu anaterodi.

Kumachititsa mtendere,

Umenewu ngwabwino.

Anakhazika chitsanzo.

Anakondwa nakodi

Kugonjera kwa Mulungu

Ndi kumutumikira.

3. Mwanzeru titsogolere

Mu kulemekezana

Ndi kudziŵa kuti Yesu

Anafera abale.

Abalewo nga Mulungu;

Awapatsa maluso.

Tiyeni tidzichepetse

Tikhale auzimu.

4. Lamulo la umutulo

Lithandiza kudziŵa

Kudzichepetsadi tokha

Ndi kusonya chikondi.

Mzimu wa Ya ngopezeka

Kuti utithandize.

Unansi wabwino ndi Ya

Udzatichepetsabe.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena