Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 197
  • Imbirani Yehova!

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Imbirani Yehova!
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Nyimbo Yatsopano
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Kuimba Kwathu Kutamande Yehova
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2003
  • Nyimbo Yatsopano
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Imbirani Yehova Zitamando
    Nsanja ya Olonda—1994
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 197

Nyimbo 197

Imbirani Yehova!

(Salmo 47:6)

1. Tikuimbira Mulungu,

Ndi kuchita mwanzeru.

Molam’lidwa mwana wake

Akulamula dziko.

Tiimba mwachilakiko.

Ya wachita zambiri!

Tifuula m’chitamando

Mothirira mang’ombe.

Popeza Yesu Ndimfumu,

Anthu amuwope.

Wayamba kulamulira.

Timudziŵikitsa.

2. Tiri munthaŵi zozunza,

zowawa ndi nsautso;

Zonga nthaŵi yachisanu,

Yokhala ngati bwinja.

Zaka chikwi zayandika;

Kuipa kudzachoka.

Kudzakhala Paradaiso.

Onse adzakondwera.

Zinthu zonse zatsopano

Tizidikiratu.

Kudziŵa chiyembekezo

Tsata chilungamo.

3. Ya akuchita zamphamvu.

Anthu achita mantha

Mmene asamalirira

Ntchito yofalitsayo.

Ambuye Mfumu ya dziko,

Apatsa madalitso.

Tiyeni timuimbire.

Kuchokera mumtima.

Abale okondedwanu,

Titametu M’lungu.

Ali pampando woyera;

Ulemu ndiwake.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena