Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 201
  • Kukondwera ndi Mtundu wa Mulungu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kukondwera ndi Mtundu wa Mulungu
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Mtundu Woyera wa Yehova
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Nyimbo kwa Wammwambamwambayo
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Moyo Wosatha Ulonjezedwa
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 201

Nyimbo 201

Kukondwera ndi Mtundu wa Mulungu

(Salmo 106:5)

1. Mwa kulalika Ufumu

Tikufunafuna anthu:

“Idzani mumve uthenga.

Wa chowonadi cha Baibulo.”

Ya aitanatu,

Athawe tsoka lowopsa,

Kumka kuchisangalalo,

m’Dziko Latsopano loikidwa.

(Korasi)

2. Wonani! ‘Mtundu woyera’

Woikidwa ndi Yehova

Mopatulidwa mukhola,

Kulengezatu chipulumutso.

Ya akondwa nafe

Ngati tichita zabwino,

Kutsanzira Kristu wathu;

Tisachoke m’njira ya Mulungu.

(Korasi)

3. Mudzikotu labwinodi,

Mopanda zinthu zovuta,

Wonani! Khamu lokondwa

Muntchito ya Mulungu ya phindu.

Sausanso mtima.

Akupeza chowonadi,

Nachigwiritsira ntchito,

Alemekeza dzina lakelo.

(KORASI)

Idzani mukondwere!

Ndi “mtundu” wa M’lungu

Nenani mbiri yabwinoyi.

Mgwadireni Mulungu.

M’lambireni ndithu.

Mukhale kumbali Yaufumu.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena