Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 88
  • Pemphero la Mtumiki wa Mulungu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Pemphero la Mtumiki wa Mulungu
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Pemphero la Mtumiki wa Mulungu
    Imbirani Yehova
  • Tiyamika Wotipatsa Moyo
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Kristu Chitsanzo Chathu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Kuyenda m’Dzina la Mulungu Wathu
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 88

Nyimbo 88

Pemphero la Mtumiki wa Mulungu

(Yakobo 3:17)

1. Atate wakumwamba,

Titame dzina lanu;

Zifundo zikhalitsa,

Zokhulupirikabe.

Zokhulupirikabe,

Inde, zimakhalitsa.

2. Pochita utumiki,

Tiphunzitseni M’lungu.

Malamulo tisunga,

Pokhalatu ndi “nkhosa.”

Pokhalatu ndi “nkhosa,”

Malamulo tisunga.

3. Tigaŵireni nzeru,

Yodzadza ndi chikondi.

Tikhale achifundo,

Ndipo opanda tsankho.

Monga opanda tsankho,

Tikhale achifundo.

4. Tikhale achimwemwe

Muutumiki wanu.

Kupempha sitileka

Muwonjeze Ufumu.

Muwonjeze Ufumu,

Kupempha sitileka.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena