Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 141
  • Mtundu Woyera wa Yehova

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mtundu Woyera wa Yehova
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Kukondwera ndi Mtundu wa Mulungu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Mvetserani Mbiri ya Ufumu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Nyimbo kwa Wammwambamwambayo
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Chifukwa cha Kukondwera cha Ziyoni
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 141

Nyimbo 141

Mtundu Woyera wa Yehova

(Yesaya 66:8)

1. Padziko mtundu unabadwa

Kwa Yehovayo m’tsiku lathu.

Wavalitsidwa mwachiyero,

Ulambira motheratu.

(Korasi)

2. Mokondwa mtundu woyerawu

Ulengeza dzina la M’lungu.

Monga chizindikiro chawo

Amalengeza Ufumu.

(Korasi)

3. Mtundu wa Yehova Ngwokondwa

Nkhosa zina ziima nawo.

Amatumikira pamodzi

Akhala m’chiyanjo cha Ya.

(KORASi)

Nkokwezekadi, sikungaime,

Kulambirako m’Ziyoni.

Mtundu wake ndi ‘khamulo’

Amasangalatsa Yehova.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena