Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 87
  • Chakudya Chamadzulo cha Ambuye

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Chakudya Chamadzulo cha Ambuye
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Mgonero wa Ambuye
    Imbirani Yehova
  • Chakudya Chamadzulo cha Ambuye
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • “Muzichita Zimenezi Pondikumbukira”
    Nsanja ya Olonda—2013
  • N’chifukwa Chiyani Tiyenera Kuchita Chikumbutso cha Mgonero wa Ambuye?
    Nsanja ya Olonda—2003
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 87

Nyimbo 87

Chakudya Chamadzulo cha Ambuye

(1 Akorinto 11:23-26)

1. Yehova Tate wakumwamba,

Usiku wopatulika!

Pa Nisani khumi ndi chinayipo,

Panali ulemelero.

Mwanawankhosa anadyedwa,

Israyeli namasuka.

Mbuye wathu anakhetsa mwazi wake

Kukwaniritsa ulosiwo.

2. Tasonkhana pamaso panu,

Tadza monga nkhosa zanu,

Kutamanda chikondi chachikulu

Chomwe chinadzetsa Kristu.

Patsogolo pathupa pali

Gome la vinyo ndi mkate.

Tidziŵa izo ndizo zizindikiro

Za chakudya chomwe tidzidya.

3. Mkatewo ndi thupi la Kristu

Loperekedwa kwa ife.

Chikho ndi chizindikiro cha mwazi

Woombola anthu ife.

Tisunge Chikumbutso ichi

M’maganizo ndi mitima.

Tikayenda mofanafana ndi Kristu,

Tidzapeza moyo wosatha.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena